Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/10 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 12

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 12
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JULY 12
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 7/10 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa July 12

MLUNGU WOYAMBIRA JULY 12

Nyimbo Na. 32

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 9, ndime 13-21 ndi bokosi patsamba 104

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mafumu 9-11

Na. 1: 1 Mafumu 9:10-23

Na. 2: Kodi Baibulo Limanena Chiyani pa Nkhani Yofunafuna Chuma ndi Kumwa Kwambiri Zoledzeretsa? (rs tsa. 171 ndime 4 ndi 5)

Na. 3: Mmene Akhristu Enieni Amasonyezera Nzeru Yochokera Kumwamba (Yak. 3:17)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 39

Mph. 5: Zilengezo.

Mph . 20: “Misonkhano Yachigawo Ndi Nthawi Imene Timalambira Mulungu Mosangalala.” Nkhani yokambirana mwa mafunso ndi mayankho. Ngati nthawi ilipo kambirananinso mfundo zazikulu m’nkhani yakuti “Zofunika Kukumbukira pa Msonkhano Wachigawo,” imene ili patsamba 6.

Mph . 10: “Ntchito Yathu Yaikulu.” Nkhani yokambirana mwa mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 55

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena