Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/10 tsamba 8
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 2
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 2
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 7/10 tsamba 8

Ndandanda ya Mlungu wa August 2

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 2

Nyimbo Na. 17

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 10, ndime 9-15 ndi bokosi patsamba 114

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mafumu 18-20

Na. 1: 1 Mafumu 18:21-29

Na. 2: Kodi Mawu Akuti Kumwamba ndi Dziko Lapansi Zidzachoka Amatanthauza Chiyani? (Chiv. 21:1)

Na. 3: Kodi Tiyenera Kupewa Makhalidwe Otani Amene Amasonyeza Mzimu Wodziimira Pawekha? (rs tsa. 173 ndime 2-8)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 15

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Njira Zowonjezera Utumiki Wanu—Gawo 4. Nkhani yochokera m’buku la Gulu, tsamba 116, ndime 1-4. Funsani wofalitsa mmodzi kapena awiri amene amathandiza Gulu Lomanga Nyumba za Ufumu kuti afotokoze chimene chimawasangalatsa ndi utumiki umenewu.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Zokumana Nazo Poyambitsa Maphunziro a Baibulo. Kukambirana ndi omvera. Fotokozani zimene zachitika m’gawo lanu patsiku lapadera loyambitsa maphunziro a Baibulo. Pemphani omvera kunena zimene akumana nazo. Sonyezani chitsanzo cha chokumana nacho chosangalatsa chimodzi kapena ziwiri. Malizani ndi kusonyeza chitsanzo cha mmene tingayambitsire phunziro pa ulendo woyamba.

Nyimbo Na. 24

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena