Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/10 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 8

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 8
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 8
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 11/10 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa November 8

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 8

Nyimbo Na. 18

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

lv mutu 14 ndime 15-19, ndi bokosi la patsamba 167

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mbiri 21-25

Na. 1: 1 Mbiri 22:11-19

Na. 2: Kodi Tingatani Kuti Tipitirize Kukonda Kwambiri Choonadi?

Na. 3: Kodi Mboni za Yehova Zimadziwa Bwanji Mfundo za M’Baibulo Zimene Zimaphunzitsa? (rs tsa. 276 ndime 1-4)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 37

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 15: Kodi Mumaopa Akufa? Nkhani yokambirana ndi omvera yochokera mu Nsanja ya Olonda ya January 1, 2009, tsamba 11 mpaka 13. Pemphani omvera kuti afotokoze ubwino wodziwa zoona zenizeni zokhudza akufa.

Mph. 15: “M’minda Mwayera Kale Ndipo M’mofunika Kukolola.” Nkhani ya mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 44

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena