Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/10 tsamba 8
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
Utumiki Wathu wa Ufumu—2010
km 11/10 tsamba 8

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Pa July 23-25, 2010, tinali ndi msonkhano wachigawo ku Civo Stadium ndipo msonkhanowu unalumikizidwa pa telefoni ndi msonkhano umene unachitikira ku Kamuzu Stadium ku Blantyre ndi ku Mzuzu Stadium ku Mzuzu. Pa msonkhanowu m’bale Gerrit Lösch wa m’Bungwe Lolamulira anatulutsa Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika la m’Chichewa. Chiwerengero cha anthu amene anapezeka pa misonkhano yonse itatuyi chinali 56,295 ndipo panabatizidwa anthu 487.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena