Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/11 tsamba 8
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 3/11 tsamba 8

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Kuyambira pa December 13, 2010 mpaka pa January 9, 2011, m’Malawi muno mwakhala mukuchitika Sukulu za Utumiki wa Ufumu zokwana 54 za akulu ndi atumiki othandiza. Akulu oposa 5,500 ndi atumiki othandiza okwana 4,900 apindula ndi maphunziro amenewa. Zimenezi zichititsa kuti mipingo imene abale amenewa akutumikiramo ipindule. Kunena zoona, atate wathu wachikondi Yehova amasamaliradi anthu ake.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena