Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/11 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa April 11

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa April 11
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 11
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 4/11 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa April 11

MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 11

Nyimbo Na. 44 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 5 ndime 9-15 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yobu 21-27 (Mph. 10)

Na. 1: Yobu 25:1–26:14 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Mtanda Suyenera Kugwiritsidwa Ntchito Polambira? (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Yesu Khristu Ndi Mikayeli Mkulu wa Angelo Ndi Munthu Mmodzi?—rs tsa. 432 ndime 1-3 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 45

Mph. 5: Zilengezo. Uzani mpingo mmene ntchito yoitanira anthu ku Chikumbutso ikuyendera pa mpingo wanu.

Mph. 15: Mmene Tingalalikirire Pogwiritsa Ntchito Kalata. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 71-73.

Mph. 15: “Umboni Wamphamvu Udzaperekedwa.” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 8 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena