Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/11 tsamba 4
  • Kulemekeza Yehova Ndi Zinthu Zathu Zamtengo Wapatali

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kulemekeza Yehova Ndi Zinthu Zathu Zamtengo Wapatali
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 5/11 tsamba 4

Kulemekeza Yehova Ndi Zinthu Zathu Zamtengo Wapatali

N’zosangalatsa kuona mmene mzimu wa Yehova ukulimbikitsira anthu, ngakhale ana kuthandiza pa ntchito yake. M’mbuyomu, kamnyamata kena ka zaka 9 kochokera ku mpingo wa Chirimba North, kanapita kukaona ofesi yathu ya nthambi ku Lilongwe. Iye analimbikitsidwa kwambiri chifukwa cha zimene anaona moti atabwerera kunyumba, anatumiza K1,000 yothandizira pa ntchito ya padziko lonse. Makolo ake ndi amene anam’patsa ndalamazi atakamba bwino nkhani m’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu. M’malo mogula zofuna zake, anatumiza ndalamazi kuti zithandizire pa ntchito yolalikira. Zimene mwana ameneyu anachita ndi chitsanzo chabwino kwambiri kwa tonsefe.—2 Akor. 9:7.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena