Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/11 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 13

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 13
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 13
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 6/11 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa June 13

MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 13

Nyimbo Na. 40 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 8 ndime 10-17 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Masalimo 38-44 (Mph. 10)

Na. 1: Salimo 41:1– 42:5 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Zimene Tingaphunzire kwa Anthu Ogwirizana Kwambiri Otchulidwa M’Baibulo Ndiponso pa Makhalidwe Awo (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Maulosi Onena za Kubwezeretsedwa kwa Aisiraeli Akukwaniritsidwa kwa Ndani Masiku Ano?—rs tsa. 46 ndime 3 mpaka tsa. 47 ndime 2 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 36

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Njira Zolalikirira Uthenga Wabwino: Kuchititsa Maphunziro a Baibulo a Panyumba. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Gulu, tsamba 98 ndime 1 mpaka tsamba 99 ndime 1. Pemphani omvera kuti afotokoze mmene amasangalalira chifukwa chophunzitsa munthu choonadi ndiponso kumuona akupita patsogolo mwauzimu. Mungapempheretu munthu mmodzi kapena awiri kuti adzayankhepo.

Mph. 10: Kodi Malamulo Achikhristu pa Nkhani ya Kukwatira, Kuthetsa Banja ndi Kupatukana ndi Otani? Nkhani yokambidwa ndi mkulu yochokera m’buku la Gulu, tsamba 194 mpaka 195, funso 1 mpaka 3.

Mph. 10: “Kuleza Mtima N’kofunika Kwambiri pa Utumiki Wathu.” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 45 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena