Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/11 tsamba 8
  • Zilengezo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zilengezo
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 8/11 tsamba 8

Zilengezo

◼ Mabuku ogawira m’mwezi wa August: Gawirani kabuku kalikonse kamasamba 32 kamene anthu angachite nako chidwi m’gawo lanu monga: Boma Limene Lidzabweretsa Paradaiso, Dikirani!, Kodi Mulungu Amatisamaliradi?, Mizimu ya Akufa—Kodi Ingakuthandizeni Kapena Kukuvulazani? Kodi Iyo Ilikodi?, Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha! ndi kakuti, “Tawonani! Ndikupanga Zinthu Zonse Zatsopano.” September: Gawirani buku lakuti Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni? Yesetsani kuyambitsa maphunziro a Baibulo pa ulendo woyamba. October: Gawirani magazini a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! Ngati mwininyumba wasonyeza chidwi, m’gawireni kapepala kakuti Kodi Mukufuna Kudziwa Choonadi? Yesetsani kuyambitsa phunziro la Baibulo. November: Gawirani kabuku kakuti Kodi Baibulo Lili ndi Uthenga Wotani? Kapena mungagawire kabuku kalikonse pa timabuku tamasamba 32 timene tatchulidwa kumayambiriroku, togawira mu August 2011.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena