Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/11 tsamba 8
  • Ndandanda ya Mlungu wa September 5

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa September 5
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 5
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 8/11 tsamba 8

Ndandanda ya Mlungu wa September 5

MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 5

Nyimbo Na. 2 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 12 ndime 8-14 (Mph. 25)

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

Kuwerenga Baibulo: Salimo 119 (Mph. 10)

Na. 1: Salimo 119:49-72 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Malemba Amatilimbikitsa Kuti Tiziopa Yehova?—Deut. 5:29 (Mph. 5)

Na. 3: Ufumu wa Mulungu Udzaukitsa Akufa—rs tsa. 379 ndime 6 –tsa. 380 ndime 2 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 12

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Machitidwe 5:17-42. Kenako, kambiranani mmene nkhani imeneyi ingatithandizire pa utumiki wathu.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Konzekerani Utumiki ndi Banja Lanu. Kufunsa komanso chitsanzo. Funsani mabanja awiri, banja lina likhale la mwamuna ndi mkazi yekha ndipo linalo likhale loti lili ndi ana. Mabanjawa afotokoze mmene amakonzekerera utumiki wakumunda pa nthawi ya Kulambira kwa Pabanja. Kenako mutu wabanja mmodzi ndi banja lake achite chitsanzo chosonyeza mmene angachitire pokonzekera utumiki wa Loweruka.

Nyimbo Na. 41 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena