Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/11 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 17

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 17
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 17
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 10/11 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa October 17

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 17

Nyimbo Na. 21 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 14 ndime 10-16 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Miyambo 12-16 (Mph. 10)

Na. 1: Miyambo 15:1-17 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Mapemphero Ovomerezeka Ali Ngati Zofukiza Zonunkhira Bwino kwa Yehova?—Sal. 141:2; Chiv. 5:8 (Mph. 5)

Na. 3: N’chiyani Chimene Chikusonyeza Kuti Tikukhala M’masiku Otsiriza?—rs tsa. 261 ndime 2 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 12

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Mateyu 5:11, 12, 14-16, 23, 24. Kambiranani mmene mavesi amenewa angatithandizire mu utumiki.

Mph. 10: Lolani Kuti Mwininyumba Aone Yekha. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 145. Chitani chitsanzo chachidule chosonyeza wofalitsa akupitanso kwa munthu amene anachita chidwi, koma m’Baibulo lake anachotsamo dzina la Mulungu.

Mph. 10: “Musalephere Kulalikira.” Mafunso ndi mayankho. Pemphani achikulire komanso ana kuti afotokoze zimene anakumana nazo polalikira ali kusukulu.

Nyimbo Na. 19 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena