Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/11 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 24

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 24
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 24
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 10/11 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa October 24

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 24

Nyimbo Na. 5 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 14 ndime 17-21 ndi bokosi patsamba 149 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Miyambo 17-21 (Mph. 10)

Na. 1: Miyambo 17:21–18:13 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Nkhondo ndi Kusowa kwa Chakudya Kuli Mbali ya “Chizindikiro”?—rs tsa. 262 ndime 1 mpaka tsa. 263 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Anthu Amene Amatamanda Chilengedwe Koma Osati Mlengi Amasonyeza Kuti Ndi Otani?—Aroma 1:20 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 15

Mph. 10: Zilengezo. Tchulani mabuku ogawira m’mwezi wa November, ndipo chitani chitsanzo chimodzi kapena ziwiri za mmene tingagawirire mabukuwa.

Mph. 25: “Kodi Mukuchita Zonse Zimene Mungathe Kuti Muphunzire Zambiri Kwa Yehova?” Mafunso ndi mayankho. Funsani mwachidule m’bale amene anaphunzitsidwa zinthu zina mwapadera ndi gulu la Yehova.

Nyimbo Na. 9 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena