Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/11 tsamba 8
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 10/11 tsamba 8

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

M’madera amene timakhala, nthawi zonse anthu amachita chidwi ndi Nyumba zathu za Ufumu. Pomanga nyumbazi, anthu ambiri ankayamikira abale athu chifukwa chogwira ntchito mogwirizana komanso modzipereka. Izi n’zimene zinachitikanso pamene abale ankamanga Nyumba ya Ufumu ya Namphiri ku dera la C-15 ku Ntcheu. Ndife osangalala kukudziwitsani kuti pamene timafika kumapeto kwa mwezi wa May, 2011, tinali titamanga Nyumba za Ufumu zokwana 1,018 m’Malawi muno. Yehova, yemwe ndi Womanga Wamkulu, ndi amene ali woyenera kutamandidwa chifukwa cha zimenezi.—Sal. 127:1.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena