Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/11 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 14

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 14
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 14
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 11/11 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa November 14

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 14

Nyimbo Na. 6 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 15 ndime 17-20 ndi bokosi patsamba 160 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Mlaliki 1-6 (Mph. 10)

Na. 1: Mlaliki 6:1-12 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Kuwonjezeka kwa Kusamvera Malamulo Kukusonyeza Chiyani?—rs tsa. 264 ndime 2 ndi 3 (Mph. 5)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Akhristu Amatsatira Malangizo a pa Aroma 12:19? (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 13

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kodi Mumasangalala Ndi “Mwayi Wopereka Nawo Mphatso Zachifundo”? Nkhani yokambidwa ndi mkulu yochokera mu Nsanja ya Olonda ya November 15, 2011, tsamba 22-23.

Mph. 15: “Tizichita Maulendo Obwereza kwa Anthu Amene Anasonyeza Chidwi.” Mafunso ndi mayankho. Mukamaliza kukambirana ndime yachitatu, chitani chitsanzo chosonyeza wofalitsa akulankhula yekha pokonzekera ulendo wobwereza. Iye akuonanso zimene analemba zokhudza munthuyo ndipo akuganizira zimene akayankhe pa funso limene anafunsa ndiponso zimene angachite kuti akayambitse phunziro pogwiritsa ntchito buku la Baibulo Limaphunzitsa Chiyani. Kambiranani mwachidule mfundo zopezeka patsamba 85 ndime 3 m’buku la Gulu, za mmene timachitira ulendo wobwereza.

Nyimbo Na. 44 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena