Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/11 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 12

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 12
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 12
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 12/11 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa December 12

MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 12

Nyimbo Na. 30 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 17 ndime 1-9 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yesaya 6-10 (Mph. 10)

Na. 1: Yesaya 6:1-13 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: N’chifukwa Chiyani Mulungu Walola Kuti Padutse Nthawi Yaitali Chonchi Asanawononge Oipa?—rs tsa. 268 ndime 2 mpaka 4 (Mph. 5)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Chikondi Sichitha?—1 Akor. 13:8; 1 Yoh. 4:8 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 36

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 15: Sukulu ya Utumiki wa Mulungu ya 2012. Nkhani yokambidwa ndi woyang’anira sukulu. Pogwiritsa ntchito ndandanda ya 2012, kambiranani mfundo zimene mukuona kuti zingathandize kwambiri mpingo wanu. Fotokozani udindo wa mlangizi wothandiza. Limbikitsani onse kuchita khama kukwaniritsa mbali zawo, kutenga nawo mbali pa mfundo zazikulu, komanso kugwiritsa ntchito malangizo ochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki amene amaperekedwa mlungu uliwonse.

Mph. 15: “Tizikhala Okonzeka Kulalikira Nthawi Zonse.” Mafunso ndi mayankho. Mukamakambirana ndime 2, funsani wofalitsa amene amachita ulaliki wamwamwayi mogwira mtima kuti afotokoze mmene amakonzekerera komanso afotokoze chokumana nacho chosangalatsa.

Nyimbo Na. 24 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena