Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/12 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 9

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 9
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 9
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 1/12 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa January 9

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 9

Nyimbo Na. 5 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cf mutu 18 ndime 10-18 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yesaya 29-33 (Mph. 10)

Na. 1: Yesaya 30:15-26 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Anthu Analengedwa Kuti Azikhala Ndi Moyo Nthawi Yochepa, Kenako N’kufa?—rs tsa. 291 ndime 2-4 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Anthu Opanda Ungwiro Angayeretse Bwanji Dzina la Yehova?—Mat. 6:9 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 61

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Muzilalikira Anthu Amene Amalankhula Chinenero China. Nkhani yochokera patsamba 2 la kabuku ka Uthenga Wabwino wa Anthu a Mitundu Yonse. Chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingagwiritsire ntchito kabukuka.

Mph. 10: Umboni Wakuti Baibulo Ndi Louziridwa Ndi Mulungu. Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Kukambitsirana, tsamba 54 ndime 3, mpaka tsamba 58 ndime 2.

Mph. 10: “Muziponya Nkhonya Zanu Mwanzeru.” Mafunso ndi mayankho. Mukamakambirana ndime 2, funsani mwachidule woyang’anira utumiki kuti afotokoze malo amene mungapeze anthu ambiri ndiponso nthawi yake mkati mwa mlungu, m’gawo la mpingo wanu.

Nyimbo Na. 115 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena