Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/12 tsamba 8
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 3/12 tsamba 8

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Yehova ndi Mulungu wopanda tsankho ndipo amafuna kuti “anthu, kaya akhale a mtundu wotani, apulumuke” ngakhalenso akhungu. (1 Tim. 2:3, 4) Umboni wa zimenezi ndi wakuti tsopano tili ndi mipingo isanu ya Chinenero Chamanja. M’mipingo imeneyi muli ofalitsa okwana 190. Tilinso ndi timagulu tachinenero chamanja ku Kasungu, Mchinji, Mangochi, Mulanje ndi Nchalo. Apainiya apadera anatumizidwa kukathandiza ena mwa magulu amenewa kuti apite patsogolo. Mosakayikira, Yehova akudalitsa kwambiri gawo la chinenero chamanja m’Malawi muno.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena