Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/12 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 5/12 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palemba la Mika 5:5 pali mawu akuti: “Tidzamutumizira abusa 7, inde atsogoleri 8 a anthu kuti akathane naye.” Sukulu Yophunzitsa Baibulo ya Abale Osakwatira ikuthandiza kwambiri pokwaniritsa ulosi umenewu m’Malawi muno. Tangoganizani. Makalasi 13 achitika kale pasukuluyi moti abale okwana 343 aphunzira kale pasukuluyi. Abale amenewa akutumikira m’mipingo yosiyanasiyana. Ena ndi apainiya othandiza ndipo ena ndi apainiya apadera m’mipingoyo. Kunena zoona, timathokoza kukhala ndi abale amene anapita kusukulu imeneyi m’mipingo yathu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena