Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/12 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 11

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 11
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 11
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 6/12 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa June 11

MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 11

Nyimbo Na. 31 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 7 ndime 9-13 ndi bokosi patsamba 56 (Mph. 25)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Maliro 1-2 (Mph. 10)

Na. 1: Maliro 2:11-19 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Anthu “Akuwononga Dziko Lapansi” Motani?—Chiv. 11:18 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Akhristu a M’nthawi ya Atumwi Ankalemekeza Mariya Mwapadera?—rs tsa. 259 ndime 3–tsa. 260 ndime 3 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 134

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Kodi Tinachita Zotani? Nkhani yokambirana yokambidwa ndi mlembi. Fotokozani zimene mpingo unachita pa nyengo ya Chikumbutso. Yamikirani abale ndi alongo chifukwa cha zimene anachita pa nyengoyi. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene anasangalala nazo pamene ankagawira mapepala oitanira anthu ku Chikumbutso. Komanso afotokoze zimene anasangalala nazo pokambirana ndi anthu atsopano amene anabwera ku Chikumbutso. Abale ndi alongo amene anachita upainiya wothandiza anganene zimene zinawasangalatsa pamene ankachita upainiyawu pa nyengoyi.

Mph. 20: “Zifukwa 12 Zimene Zimatichititsa Kulalikira.” Nkhani yokambirana.

Nyimbo Na. 47 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena