Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/12 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 16

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 16
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JULY 16
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 7/12 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa July 16

MLUNGU WOYAMBIRA JULY 16

Nyimbo Na. 75 ndi Pemphero

❑ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 9 ndime 1-7 ndi mabokosi a patsamba 68 ndi 70 (Mph. 25)

❑ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Ezekieli 15–17 (Mph. 10)

Na. 1: Ezekieli 16:14-27 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Choonadi Chimene Yesu Ankanena pa Yohane 18:37 N’chiyani? (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Yesu Ndi Amene Anayambitsa Mwambo wa Misa?—rs tsa. 282 ndime 4 mpaka tsa. 284 ndime 4 (Mph. 5)

❑ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 119

Mph. 5: Zilengezo.

Mph. 10: Sukulu ya Utumiki wa Mulungu Ikuthandizeni Kupita Patsogolo Mwauzimu. Nkhani yokambidwa ndi woyang’anira Sukulu ya Utumiki, yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki, tsamba 6 ndime 1 mpaka kumapeto kwa tsamba 8. Funsani wofalitsa mmodzi kapena awiri kuti afotokoze mmene sukuluyi yawathandizira mu utumiki.

Mph. 20: “Thandizani Anthu Kumvera Mulungu.” Mafunso ndi mayankho. Mukamakambirana ndime yachisanu, chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingagawirire kamodzi ka timabuku tathu. Mukamaliza kukambirana ndime 6, chitani chitsanzo cha mphindi zitatu chosonyeza wofalitsa akuchititsa phunziro la Baibulo pogwiritsa ntchito kabuku kakuti, Mverani Mulungu ndipo akambirane zithunzi za patsamba 4.

Nyimbo Na. 120 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena