Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/12 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 9/12 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Kuyambira m’mwezi wa May mpaka mwezi wa July chaka chino, akulu onse m’Malawi muno anali pa “Sukulu ya Akulu” ya masiku anayi ndi hafu. Mosakayikira, malangizo amene akulu analandira kusukuluyi awathandiza kuweta mwachikondi nkhosa zimene Mulungu anawaikiza. (Mac. 20:28) Tikuthokoza Yehova ndiponso gulu lake pothandiza kuti sukuluyi iyende bwino m’gawo la nthambi yathu. Tikuthokozanso abale nonse chifukwa cha zopereka zanu zimene zinathandiza kuti sukuluyi iyende bwino m’dera lanu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena