Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/12 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 8

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 8
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 8
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 10/12 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa October 8

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 8

Nyimbo Na. 26 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 13 ndime 8-16, ndi bokosi patsamba 105 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Danieli 7-9 (Mph. 10)

Na. 1: Danieli 7:13-22 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Baibulo Limasonyeza Kuti AKhristu Oona Ndi Gulu Lochita Zinthu Mwadongosolo?—rs tsa. 141 ndime 2 mpaka tsa. 142 ndime 2 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Yehova ndi Wokhulupirika M’njira Ziti?—Chiv. 15:4; 16:5 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 133

Mph. 10: Ngati Wina Wanena Kuti ‘Ndine Wotanganidwa.’ Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Kukambitsirana, tsamba 19, ndime 5 mpaka tsamba 20 ndime 4. Kambiranani zina mwa mfundo zimene zili m’bukuli komanso mfundo zina zimene zakhala zothandiza m’gawo la mpingo wanu. Chitani zitsanzo ziwiri zachidule.

Mph. 10: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Mateyu 21:12-16 ndi Luka 21:1-4. Kambiranani zimene tikuphunzira pa nkhani zimenezi.

Mph. 10: “Yesetsani Kumalalikira Madzulo.” Mafunso ndi mayankho. Mukamakambirana ndime yachiwiri, pemphani omvera kuti afotokoze zinthu zosangalatsa zimene anakumana nazo pamene ankalalikira nthawi yamadzulo.

Nyimbo Na. 92 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena