Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/12 tsamba 8
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 10/12 tsamba 8

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

M’mwezi wa March chaka chino, m’Malawi muno tinachititsa maphunziro a Baibulo okwana 106,307. Zimenezi zikusonyeza kuti chiwerengero cha Mboni chikhoza kuwonjezeka kwambiri m’gawo la nthambi yathu. Tikukuthokozani nonsenu chifukwa cha khama lanu. Choncho tiyeni tichite zonse zimene tingathe kuti tipitirize kuthirira mbewu za choonadi zimene tinabzala m’mitima ya anthu pa nyengo ya Chikumbutso.—1 Akor. 3:6.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena