Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/12 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 12

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 12
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 12
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 11/12 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa November 12

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 12

Nyimbo Na. 118 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 15 ndime 1-7 ndi bokosi patsamba 116 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Amosi 1-9 (Mph. 10)

Na. 1: Amosi 3:1-15 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi “Chipangano Chatsopano” Chimanena Kuti Dziko Lapansi Lidzakhala Paradaiso Ngati Mmene “Chipangano Chakale” Chimanenera?—rs tsa. 336 ndime 1-3 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Kumvetsa Bwino Lemba la Salimo 51:17 Kungatithandize Bwanji? (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 68

Mph 10: Ngati Wina Atanena Kuti, ‘Simumakhulupirira Yesu.’ Nkhani yokambirana yochokera m’buku la Kukambitsirana tsamba 433, ndime 1 mpaka 3. Chitani chitsanzo chimodzi chachidule.

Mph 10: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Maliko 1:16-20. Kambiranani mmene malemba amenewa angatithandizire mu utumiki wathu.

Mph 10: “Muzisangalala Chifukwa Chogwira Ntchito Mwakhama.” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 98 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena