Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/13 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 14

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 14
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 14
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 1/13 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa January 14

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 14

Nyimbo Na. 103 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 17 ndime 15-19 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Mateyu 7-11 (Mph. 10)

Na. 1: Mateyu 10:24-42 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Muzichita Zinthu Mwanzeru Ndipo Muzipewa Zinthu Zopanda Pake—1 Sam. 12:21; Miy. 23:4, 5 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Ndi Zinthu Ziti Zimene Tiyenera Kutchula Tikamapemphera?—rs tsa. 341 ndime 8–tsa. 342 ndime 6 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 73

Mph. 10: Athandizeni pa Zosowa Zawo. Nkhani yochokera m’buku la Sukulu ya Utumiki tsamba 188, ndime 4 mpaka tsamba 189, ndime 4. Funsani mwachidule munthu amene anapita patsogolo chifukwa chakuti anthu ena anamusonyeza chidwi.

Mph. 10: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Mateyu 4:1-11. Kambiranani mmene malemba amenewa angatithandizire mu utumiki wathu.

Mph. 10: “Perekani Umboni Mokwanira.” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 92 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena