Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/13 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa January 21

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa January 21
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 21
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 1/13 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa January 21

MLUNGU WOYAMBIRA JANUARY 21

Nyimbo Na. 40 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 18 ndime 1-5, bokosi patsamba 142, 144. (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Mateyu12-15 (Mph. 10)

Na. 1: Mateyu 14:23–15:11 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Ngati Wina Wanena Kuti, ‘Ngati Mukufuna Kundilalikira Uthenga Wanu, Mupemphere Kaye’—rs tsa. 342 ndime 7-8 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani pa Chitsanzo cha Isaki Chokonda Kuchita Zinthu Mwamtendere?—Gen. 26:19-22 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 32

Mph. 10: Lengezani Uthenga Wabwino Mwakhama. (Mac. 5:42) Funsani wofalitsa m’modzi kapena awiri amene amadziwika kuti amalalikira mwakhama. N’chiyani chimawathandiza kuti aziona utumiki kukhala wofunika? Kodi amachita zotani pokonzekera utumiki? Kodi utumiki wawathandiza bwanji kuti akhale paubwenzi wolimba ndi Yehova?

Mph. 10: Khalidwe Lathu Labwino Limapereka Umboni. (1 Pet. 2:12) Nkhani yokambirana ndi omwera yochokera m’buku lakuti Khalanibe M’chikondi cha Mulungu mutu 14, ndime 15 mpaka 19. Pemphani omvera kunena zimene zinawachitikira chifukwa chokhala oona mtima pa zinthu zonse.

Mph. 10: “Kodi Mungapemphe Gawo Lanulanu?” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 96 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena