Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/13 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 1/13 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

“Anthu inu tipita nanu limodzi, chifukwa tamva kuti Mulungu ali ndi inu.” (Zek. 8:23) Ulosi umenewu ukukwaniritsidwa chifukwa anthu ambiri akulowa m’gulu la anthu a Yehova. Chaka chatha panachitika misonkhano yachigawo 73 ndipo anthu amene anapezeka pamisonkhano imeneyi anali okwana 256,658. Tinasangalala kwambiri kuona anthu atsopano okwana 2,844 akubatizidwa m’madzi posonyeza kuti anadzipereka kwa Yehova.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena