Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/13 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa February 11

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa February 11
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 11
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 2/13 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa February 11

MLUNGU WOYAMBIRA FEBRUARY 11

Nyimbo Na. 8 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

bt mutu 18 ndime 19-24 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Mateyu 26-28 (Mph. 10)

Na. 1: Mateyu 27:24-44 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Kuleza Mtima Kwa Mulungu Kukuthandiza Bwanji Kuti Anthu Adzapulumuke?—2 Pet. 3:9, 15 (Mph. 5)

Na. 3: Ngati Wina Wanena Kuti, ‘Mumakonda Kunena Kwambiri za Maulosi’—rs tsa. 390 ndime 8-tsa. 391 ndime 1 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 31

Mph. 10: Kodi Tikuphunzirapo Chiyani? Nkhani yokambirana. Werengani Mateyu 6:19-21 ndi Luka 16:13. Kenako mukambirane mmene malemba amenewa angatithandizire pa utumiki wathu.

Mph. 20: “Kodi Mungachite Upainiya Wothandiza?” Nkhani ya mafunso ndi mayankho. Ikambidwe ndi woyang’anira utumiki. Mukamaliza kukambirana ndime yachiwiri, funsani mwachidule ofalitsa awiri amene akonza zochita upainiya wothandiza m’mwezi wa March. Mmodzi akhale woti ali pa ntchito yolembedwa ndipo winayo akhale woti amadwaladwala kapena ndi wokalamba. Kodi adzasintha zinthu zotani pa moyo wawo kuti adzathe kuchita upainiya? Mukamaliza kukambirana ndime yachitatu chitani chitsanzo chosonyeza mwamuna ndi mkazi wake kapena banja lokhala ndi ana likuchita kulambira kwa pabanja. Kenako akambirane zimene angachite kuti adzawonjezere utumiki wawo.

Nyimbo Na. 122 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena