Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/13 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 8/13 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Nyumba ya Ufumu ya mpingo wa Mayani Hill itamangidwa m’dera la C-19 ku Dedza, mfumu ya deralo inayamikira gulu lathu chifukwa chomanga nyumba yokongola kwambiri m’dera lake. Mfumuyi inachita chidwi ndi kukongola komanso kulimba kwa nyumbayi ndipo inanena kuti anthu amene ankagwira ntchito yomanga nyumbayi anali ogwirizana. Khalidwe limeneli linathandiza anthu a m’derali kuzindikira kuti anthuwa ndi Akhristu oona. Pofika pano Nyumba za Ufumu zoposa 1,070 zamangidwa m’Malawi muno. Koma kodi udindo wathu ndi wotani? Tiyenera kupitiriza kusamalira malo abwino olambirirapowa amene Yehova watipatsa kudzera m’gulu lake.—1 Mbiri 29:1-5, 8, 9.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena