Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/13 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 11

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 11
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 11
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 11/13 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa November 11

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 11

Nyimbo Na. 60 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 3 ndime 7 mpaka 12 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Aheberi 1-8 (Mph. 10)

Na. 1: Aheberi 4:1-16 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Tingasonyeze Bwanji Kuti Tili Ndi “Nzeru Yochokera Kumwamba”?—Yak. 3:17, 18 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Chofunikira kwa Akhristu Ndi Kukonda Anzawo Basi?—rs tsa. 88 ndime 3 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 73

Mph 10: Kodi Tingathandize Bwanji Anthu Ena? Nkhani yokambidwa ndi mkulu yochokera mu Nsanja ya Olonda ya November 15, 2013, tsamba 8 ndi 9.

Mph. 10: Kodi Tingatani Kuti Tisamachite Mantha Tikamalalikira? Nkhani yokambirana pogwiritsira ntchito mafunso awa: (1) Kodi pemphero lingatithandize bwanji ngati timachita mantha tikamalalikira? (2) N’chifukwa chiyani kukonzekera n’kothandiza kuti tisamachite mantha tikakhala mu utumiki? (3) N’chiyani chingatithandize kuti tisamachite mantha tikamalalikira ndi woyang’anira dera? (4) Kodi kuchita mantha kungatilepheretse bwanji kuchita zambiri mu utumiki? (5) Kodi n’chiyani chakuthandizani kuthetsa mantha mu utumiki?

Mph. 10: “Tengerani Chitsanzo kwa Aneneri—Hoseya.” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 113 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena