Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/13 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 18

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 18
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 18
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 11/13 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa November 18

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 18

Nyimbo Na. 104 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 3 ndime 13 mpaka 19 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Aheberi 9-13 (Mph. 10)

Na. 1: Aheberi 10:19-39 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Kodi Kukhala pa Ubwenzi Ndi Mulungu N’Kofunikadi?—rs tsa. 88 ndime 4-5 (Mph. 5)

Na. 3: Njira Zimene Tingalimbikitsire Ena—Aroma 15:4; 2 Akor. 1:3, 4 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 10

Mph. 10: Bokosi la Mafunso. Nkhani yokambirana. Kenako dziwitsani abale ndi alongo mmene ntchito yogawira Uthenga wa Ufumu Na. 38 ikuyendera pa mpingo wanu.

Mph. 10: “Tabwera Kuti . . . ” Nkhani yokambirana. Kenako, tchulani mabuku ogawira m’mwezi wa December, ndipo chitani chitsanzo chimodzi pogwiritsa ntchito mfundo za m’nkhaniyi. Kambirananinso zimene tikuphunzira pa nkhani yakuti Zochitika mu Utumiki Wakumunda patsamba 4.

Mph. 10: Yehova Amamva Mapemphero a Atumiki Ake. (1 Yohane 3:22) Nkhani yochokera mu Buku Lapachaka la 2013, tsamba 91 ndime 2 ndi 3, ndiponso tsamba 108 ndi 109. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene tikuphunzirapo.

Nyimbo Na. 56 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena