Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/13 tsamba 4
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 2
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 2
Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
km 11/13 tsamba 4

Ndandanda ya Mlungu wa December 2

MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 2

Nyimbo Na. 61 ndi Pemphero

□ Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 4 ndime 9-14 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Petulo 1 mpaka 2 Petulo 3 (Mph. 10)

Na. 1: 1 Petulo 2:18 mpaka 3:1-7 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Chipembedzo Choona Chimaphunzitsa Zimene Baibulo Limanena Komanso Chimadziwitsa Anthu Dzina la Mulungu—rs tsa. 89 ndime 3-4 (Mph. 5)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Timakhulupirira Kuti Yesu Ndi Mesiya?—Luka 24:44; Agal. 4:4 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 116

Mph. 5: Yambitsani Phunziro la Baibulo Loweruka Loyambirira. Nkhani. Limbikitsani ofalitsa onse kuti adzayesetse kuyambitsa maphunziro a Baibulo Loweruka loyambirira la mwezi wa December. Pogwiritsa ntchito tsamba lomaliza la Nsanja ya Olonda ya December, sonyezani mmene tingayambitsire phunziro la Baibulo.

Mph. 15: Kodi Mwaiyesa? Nkhani yokambirana. Kambani nkhani yofotokoza mfundo zachidule za m’nkhani zotsatirazi zomwe zili mu Utumiki Wathu wa Ufumu waposachedwapa. Nkhani zake ndi zakuti: “Webusaiti Yathu Yovomerezeka Yakonzedwa Kuti Izithandiza Ifeyo Komanso Anthu Ena” (km 12/12), “Muzigwiritsira Ntchito Mavidiyo Pophunzitsa” ndi yakuti “Kodi Ndi Ndani Amene Angakonde Magazini Awa?” (km 5/13). Pemphani omvera kuti afotokoze mmene kugwiritsa ntchito mfundo zopezeka m’nkhanizi kwawathandizira.

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Nyimbo Na. 12 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena