Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/14 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 2/14 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Pamene mapeto akuyandikira, tiyeni tipitirize kulalikira kwa anthu osiyanasiyana ndipo Yehova adzatidalitsa. Mwachitsanzo, bambo wina wa ku Lizulu anaphunzira choonadi kuchokera kwa wachibale wake. Ngakhale kuti poyamba bamboyu anali Rasi ndipo ankamwa mowa mwauchidakwa komanso kusuta fodya, ataphunzira choonadi anasintha. Iye anabatizidwa mu October 2011 ndipo mkazi wakenso anabatizidwa ku Dedza pa msonkhano wachigawo wa 2013. Panopa m’baleyu ndi mtumiki wothandiza. Kodi tikuphunzirapo chiyani? Mawu a Mulungu ali ndi mphamvu yosintha anthu. (Aheb. 4:12) Tikuphunziraponso kuti tiziyesetsa kulalikira kwa achibale athu omwe si Mboni.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena