Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/14 tsamba 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 30

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 30
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 30
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 6/14 tsamba 7

Ndandanda ya Mlungu wa June 30

MLUNGU WOYAMBIRA JUNE 30

Nyimbo Na. 51 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 13 ndime 8-13 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Levitiko 14-16 (Mph. 10)

Kubwereza za M’Sukulu ya Utumiki wa Mulungu (Mph. 20)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 58

Mph. 10: “M’pofunika Kumapitako Mwachangu.” Nkhani. Mukamaliza kukamba nkhaniyi, chitani chitsanzo chachidule chosonyeza mmene tingayambitsire maphunziro Loweruka loyamba la mwezi wa July pogwiritsa ntchito chitsanzo cha ulaliki chomwe chili patsamba 8.

Mph. 20: “Kuphunzira Patokha N’kothandiza Kwambiri.” Onani tsamba 3-4. Nkhani yokambirana. Funsani wofalitsa amene amakonda kuphunzira payekha.

Nyimbo Na. 69 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena