Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/14 tsamba 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 4

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 4
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 4
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 7/14 tsamba 7

Ndandanda ya Mlungu wa August 4

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 4

Nyimbo Na. 109 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 14 ndime 14-19 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Numeri 4-6 (Mph. 10)

Na. 1: Numeri 4:17-33 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Baibulo Limati Ena Sadzapulumutsidwa Konse—rs tsa. 95 ndime 3–tsa. 96 ndime  2 (Mph. 5)

Na. 3: Yehova Amaweruza Anthu Amene Amanamizira Ena Milandu—lv tsa. 137 ndime  11-12 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 85

Mph. 10: Zimene Munganene Pogawira Magazini a August. Nkhani yokambirana. Pogwiritsa ntchito zitsanzo za ulaliki zimene zili patsamba lino, chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingagawirire magaziniwa kumapeto kwa mlungu limodzi ndi kapepala. Kenako funsani omvera mafunso awa: N’chifukwa chiyani tiyenera kugawiranso magazini kumapeto kwa mlungu ngati pakufunika kutero? Kodi ndi nthawi iti pamene tingachite zimenezi?

Mph. 10: Zosowa za pampingo.

Mph. 10: Kodi Tinachita Zotani? Nkhani yokambirana. Pemphani omvera kuti afotokoze mmene anapindulira pogwiritsa ntchito malangizo a m’nkhani yakuti, “Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki​—Mmene Tingayambire Ulaliki Wamwamwayi.” Kenako apempheni kuti anene zinthu zosangalatsa zimene anakumana nazo.

Nyimbo Na. 75 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena