Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/14 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 18

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 18
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 18
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 8/14 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa August 18

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 18

Nyimbo Na. 92 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 15 ndime 1-6 ndi bokosi patsamba 184 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Numeri 10-13 (Mph. 10)

Na. 1: Numeri 10:1-16 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Chifukwa Chake Chikhulupiriro Chiyenera Kukhala ndi Ntchito—rs tsa. 97 ndime 1-4 (Mph. 5)

Na. 3: Dina Ndi Chitsanzo Chotichenjeza—lv tsa. 102-103 ndime 13-15 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 74

Mph. 15: “Patha Zaka 100 Tikulengeza za Ufumu.”​—Gawo 1. Nkhani yokambirana. Kambiranani ndime 1 mpaka 3. Mukakambirana funso la ndime 3, funsani ofalitsa awiri omwe akhala Mboni kwa nthawi yaitali. Apempheni kuti afotokoze zinthu zosangalatsa zimene zinawachitikira atangoyamba kumene kulalikira.

Mph. 15: “Patha Zaka 100 Tikulengeza za Ufumu.”​—Gawo 2. Mafunso ndi mayankho. Kambiranani ndime 4 mpaka 6. Mukamakambirana ndime 5, funsani apainiya okhazikika awiri kuti afotokoze zimene anachita kuti akwanitse kuyamba upainiya.

Nyimbo Na. 103 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena