Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/14 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa September 15

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa September 15
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 15
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 9/14 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa September 15

MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 15

Nyimbo Na. 131 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 1 ndime 10-17 ndi bokosi patsamba 14 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Numeri 26–29 (Mph. 10)

Na. 1: Numeri 27:​15-23 ndi 28:​1-10 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Mulungu Sanalenge Mdyerekezi—rs tsa. 354 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Kuopsa kwa Tchimo—bh tsa. 63 ndime 13-14 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 11

Mph. 15: Kodi Tinachita Zotani? Nkhani yokambidwa ndi woyang’anira utumiki. Fotokozani zimene mpingo wanu unachita mu utumiki m’chaka chautumiki chathachi komanso zimene unachita pa nthawi ya ntchito yapadera mu August. Tchulani zinthu zabwino zimene unakwanitsa kuchita, ndipo yamikirani abale ndi alongo chifukwa cha zimenezi. Pemphani omvera kuti afotokoze zinthu zosangalatsa zomwe anakumana nazo m’mwezi wa August. Komanso funsani wofalitsa amene anawonjezera zochita mu utumiki pa nthawiyi. Pomaliza, tchulani mfundo imodzi kapena ziwiri zimene mpingo wanu uyenera kuyesetsa kuti uchite bwino chaka cha utumiki talowachi. Komanso fotokozani zimene zingathandize mpingo wanuwo kuti mukwanitse kuchita zimenezi.

Mph. 15: “Tengerani Chitsanzo kwa Aneneri—Nahumu.” Mafunso ndi mayankho.

Nyimbo Na. 46 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena