Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/14 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 10/14 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

M’chaka chautumiki cha 2013, abale ndi alongo 471 anaphunzira kulemba ndi kuwerenga. Tikukuthokozani abale chifukwa chothandiza anthu amenewa. Zimenezi ziwathandiza abale athuwa kuti azitha kuphunzira choonadi paokha komanso kuti aziphunzitsa mabanja awo. Ziwathandizanso kuti azilalikira mogwira mtima anthu a mitundu yonse n’cholinga choti adziwe choonadi molondola.—1 Tim. 2:4.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena