Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/14 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 10

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 10
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 10
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 11/14 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa November 10

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 10

Nyimbo Na. 1 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 4 ndime 1-9 ndi chigawo choyamba patsamba 36 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Deuteronomo 19-22 (Mph. 10)

Na. 1: Deuteronomo 22:20-30 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Mmene Uchimo Umakhudzira Ubwenzi Wathu Ndi Mulungu—rs tsa. 361 ndime 1-4 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Baibulo Limati Chiyani pa Nkhani Yopatukana?—lv tsa. 220 ndime 2–tsa. 221 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 12

Mph. 10: Funsani Woyang’anira Utumiki. Kodi ntchito yanu ndi yotani? Mukamayendera magulu a utumiki, kodi cholinga chanu chimakhala chiyani? N’chiyani chomwe anthu a m’gululo angachite kuti apindule mukamayendera gulu lawo? Wofalitsa akakufunsani zokhudza utumiki, kodi mumamuthandiza bwanji?

Mph. 20: “Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Muzisonyeza Chidwi Munthu Amene Mukumulalikira.” Nkhani yokambirana. Mukamaliza kukambirana nkhaniyi, chitani chitsanzo cha mbali ziwiri. Mbali yoyamba, wofalitsa agawire buku kapena kapepala komwe tikugawira mwezi uno, koma asasonyeze chidwi kwa munthuyo. Mbali yachiwiri, achitenso zomwezo koma asonyeze kuti ali ndi chidwi ndi munthuyo.

Nyimbo Na. 84 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena