Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/15 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 2/15 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Chaka chatha, anthu 289,499 anabwera pa Chikumbutso cha imfa ya Yesu Khristu. Chiwerengerochi ndi chowirikiza katatu chiwerengero cha Mboni za Yehova m’Malawi muno. Tiyeni tiyesetse kuitananso anthu ambiri chaka chino kuti adzabwere pa Chikumbutso, chomwe chidzachitike pa 3 April. Anthuwa adzaphunzira za chikondi chimene Mulungu anatisonyeza anthufe komanso zimene Mulungu watilonjeza.​—Yoh. 3:16.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena