Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/15 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa April 13

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa April 13
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 13
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 4/15 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa April 13

MLUNGU WOYAMBIRA APRIL 13

Nyimbo Na. 21 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 11 ndime 9-16 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Samueli 19-22 (Mph. 8)

Na. 1: 1 Samueli 21:10-15 ndi 22:1-4 (Osapitirira mph. 3)

Na. 2: Tizilimbikitsa Ndiponso Kutonthoza Anthu mu Utumiki—bt tsa. 85-86 ndime 3-4 ndi bokosi patsamba 86 (Mph. 5)

Na. 3: N’chifukwa Chiyani Anthufe Timavutika?—igw tsa. 15 ndime 1-4 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: “Muzigwiritsa ntchito bwino nthawi yanu.”—Aef. 5:15, 16.

Nyimbo Na. 115

Mph. 10: “Muzigwiritsa Ntchito Bwino Nthawi Yanu.” Nkhani yofotokoza mutu wa mwezi uno.—Aef. 5:15, 16; onani Nsanja ya Olonda ya May 15, 2012, tsamba 19-20 ndime 11-14.

Mph. 20: “Muzigwiritsa Ntchito Bwino Nthawi Mukakhala mu Utumiki.” Nkhani yokambirana.

Nyimbo Na. 98 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena