Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/15 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 25

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 25
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA MAY 25
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 5/15 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa May 25

MLUNGU WOYAMBIRA MAY 25

Nyimbo Na. 9 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 13 ndime 11-18 (30 min.)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Samueli 13-15 (8 min.)

Na. 1: 2 Samueli 13:34–14:7 (Osapitirira 3 min.)

Na. 2: Tizikhulupirira Bungwe Lolamulira—bt tsa. 111 ndime 9-10 (5 min.)

Na. 3: Mzimu Woyera Umatithandiza Kuchita Zambiri—Eks. 35:30-35 (5 min.)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: Muzithandiza anthu onse kudziwa choonadi molondola.—1 Tim. 2:3, 4.

Nyimbo Na. 121

10 min: Funsani Woyang’anira Kagulu ka Utumiki Wakumunda. Funsani m’bale amene amayang’anira kagulu ka utumiki mafunso otsatirawa: Kodi ntchito yanu ndi yotani? Kodi mumakwanitsa bwanji kuchita maulendo a ubusa kwa anthu amene ali m’kagulu kanu? N’chifukwa chiyani n’zofunika kuti wofalitsa aliyense azikudziwitsani akasamuka kapena akasintha nambala yake ya foni? N’chifukwa chiyani akulu amakonza zoti ofalitsa azikumana m’timagulu tawo pokonzekera utumiki, m’malo mongopangira pamodzi?

20 min: “Muzithandiza Anthu Osaona Kudziwa za Yehova.” Mafunso ndi mayankho. Chitani chitsanzo chosonyeza mmene tingagwiritsire ntchito mfundo za m’nkhaniyi.

Nyimbo Na. 96 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena