Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/15 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa July 20

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa July 20
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA JULY 20
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 7/15 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa July 20

MLUNGU WOYAMBIRA JULY 20

Nyimbo Na. 26 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 16 ndime 1-9 (30 min.)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mafumu 12-14 (8 min.)

Na. 1: 1 Mafumu 12:21-30 (Osapitirira 3 min.)

Na. 2: Yehova Amadalitsa Anthu Omutumikira ndi Mtima Wonse—dp tsa. 7-8 ndime 7-11 (5 min.)

Na. 3: Kodi Baibulo Lingathandize Bwanji Amuna M’banja?—igw tsa. 26 ndime 1-2 (5 min.)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: ‘Pitani mukaphunzitse anthu kuti akhale ophunzira anga.’—Mat. 28:19, 20.

Nyimbo Na. 89

20 min: “Zithunzi Zofotokoza Nkhani ya M’Baibulo.” Nkhani yokambirana yomwe ili patsamba 3 mpaka 6. (Pitani pa jw.org/ny kuti mupange dawunilodi Utumiki Wathu wa Ufumu wa July womwe uli ndi zithunzi zofotokoza nkhani za m’Baibulo.) Ngati n’zotheka, sankhiranitu ana oti adzawerenge mawu a anthu a m’nkhaniyi ali pamalo awo. Kenako, pemphani ana angapo kuti abwere kupulatifomu kuti adzakambirane mafunso omwe ali m’bokosi lakuti, “Kodi Tikuphunzira Chiyani pa Nkhaniyi?” Muyenera kupempheratu chilolezo kwa makolo a anawo. Pomaliza limbikitsani makolo kuti azigwiritsa ntchito mabuku kapena mavidiyo a ana pothandiza ana awo kukhala ophunzira a Yesu.

10 min: Bokosi la Mafunso. Nkhani yokambirana.

Nyimbo Na. 66 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena