Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/15 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 17

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 17
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 17
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 8/15 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa August 17

MLUNGU WOYAMBIRA AUGUST 17

Nyimbo Na. 1 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 17 ndime 9-16 (30 min.)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Mafumu 1-4 (8 min.)

Na. 1: 2 Mafumu 1:11-18 (Osapitirira 3 min.)

Na. 2: Mavuto Amene Angabwere Chifukwa Chocheza ndi Anthu Olakwika—lv tsa. 102-105 ndime 13-17 (5 min.)

Na. 3: Zimene Tiyenera Kuchita Kuti Tikhale pa Ubwenzi ndi Mulungu—igw tsa. 28 ndime 5–tsa. 29 ndime 3 (5 min.)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: “Ine ndi a m’nyumba yanga, tizitumikira Yehova.”​—Yos. 24:15.

Nyimbo Na. 52

30 min: “Mawu Awa . . . Azikhala Pamtima Pako.” Mafunso ndi mayankho. Kambiranani mafunso omwe ali m’nkhaniyi. Gwiritsani ntchito mfundo za m’ndime yoyamba monga mawu oyamba ndipo mugwiritse ntchito mfundo za m’ndime yomaliza monga mawu omaliza. Ngati abale ambiri a mumpingo mwanu sangathe kuonera vidiyoyi kunyumba kwawo, kambiranani funso 3, 4, 5, 7, 9, 10 ndi 15.

Nyimbo Na. 88 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena