Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/15 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 8/15 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Kuwonjezera pa ofesi yomasulira mabuku m’Chitumbuka yomwe ili ku Mzuzu, tatsegulanso ofesi ina yomasulira mabuku m’Chitonga ku Chintheche, m’boma la Nkhatabay, komanso m’Chikyangonde, ku Karonga. Posachedwapa titsegulanso ofesi ina yomasulira mabuku m’Chiyao ku Namwera, m’boma la Mangochi. N’zodziwikiratu kuti izi zithandiza kuti anthu ambiri azimva uthenga wa m’Baibulo m’chilankhulo chawo.—Mac. 2:8, 11.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena