Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/15 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa September 14

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa September 14
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 14
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 9/15 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa September 14

MLUNGU WOYAMBIRA SEPTEMBER 14

Nyimbo Na. 114 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 18 ndime 20-24 ndi bokosi patsamba 188 (30 min.)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Mafumu 16-18 (8 min.)

Na. 1: 2 Mafumu 17:12-18 (Osapitirira 3 min.)

Na. 2: Kodi Mungatani Kuti Muzipindula Kwambiri Mukamawerenga Baibulo?—igw tsa. 32 (5 min.)

Na. 3: Muzithandiza Atumiki a Yehova Mopanda Mantha—bt tsa. 135-136 ndime 11-14 (5 min.)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: ‘Muzichitira umboni mokwanira za uthenga wabwino.’—Mac. 20:24.

Nyimbo Na. 23

10 min: ‘Muzichitira Umboni Mokwanira Uthenga Wabwino.’ Nkhani yochokera pa mutu wa mwezi uno komanso m’buku lakuti, Kuchitira Umboni, mutu 1, ndime 1-11.—Mac. 20:24.

20 min: “Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Kulalikira M’gawo Lamalonda.” Nkhani yokambirana. Chitani chitsanzo chachidule chokhala ndi mbali ziwiri. Mbali yoyamba isonyeze wofalitsa akulephera kuchita zinthu mozindikira pamene akulalikira kwa munthu wogulitsa malonda. Mbali yachiwiri isonyeze wofalitsayo akuchita zinthu mozindikira. Ndiyeno funsani omvera kuti afotokoze chifukwa chake akuona kuti m’chitsanzo chachiwirichi wofalitsayo wachita bwino.

Nyimbo Na. 96 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena