Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/15 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 9/15 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Ndife osangalala kukudziwitsani kuti kuwonjezera pa mzinda wa Blantyre ndi wa Lilongwe, tsopano tayambanso kugwiritsa ntchito dongosolo lapadera lolalikira m’malo opezeka anthu ambiri mumzinda wa Mzuzu. Munthu wina ataona zimenezi anayamikira ndipo ananena kuti: “Tsopano sindizivutikanso kupeza mabuku anu. Ndizingobwera pano kudzatenga.” Njira imeneyi ikuthandiza kuti tizilalikira kwa anthu ambiri ndipo ikuyenda bwino m’mizinda yonse ya Blantyre, Lilongwe ndi Mzuzu. Posachedwapa tiyambanso kugwira ntchitoyi mumzinda wa Zomba.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena