Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/15 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 23

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 23
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 23
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 11/15 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa November 23

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 23

Nyimbo Na. 119 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 22 ndime 1-8 (30 min.)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 2 Mbiri 1-5 (8 min.)

Na. 1: 2 Mbiri 3:14-17 mpaka 4:1-6 (Osapitirira 3 min.)

Na. 2: Yendani ndi Yehova—ia tsa. 17-19 ndime 4-8 (5 min.)

Na. 3: Kodi Kubatizidwa N’kofunika Bwanji kwa Akhristu?—bh tsa. 174-175 ndime 1-4 (5 min.)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezu Uno: “Ineyo ndinabzala, Apolo anathirira, koma Mulungu ndiye anakulitsa.”—1 Akor. 3:6.

Nyimbo Na. 47

10 min: “Kukonzekera Bwino N’kofunika Kuti Tiziphunzitsa Mwaluso.” Nkhani.

10 min: Makhalidwe Abwino Amathandiza Kuti Anthu Azimvetsera Uthenga Wathu. Nkhani yokambirana yochokera mu Buku Lapachaka la 2015 tsamba 49, ndime 3, mpaka tsamba 52, ndime 1; ndiponso tsamba 140, ndime 3, mpaka tsamba 141, ndime 3. Pemphani omvera kuti afotokoze zimene akuphunzirapo.

10 min: “Muzigwiritsa Ntchito Bwino Buku Lakuti Baibulo Limaphunzitsa Chiyani.” Nkhani yokambirana. Chitani chitsanzo chachidule.

Nyimbo Na. 123 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena