Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/15 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 11/15 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Atumiki a Yehova amachita zambiri pa nyengo ya Chikumbutso. Kutatsala miyezi 5 kuti Chikumbutso cha chaka cha 2015 chichitike, panali apainiya othandiza okwana 2,829. Koma m’miyezi ya March, April ndi May, chiwerengerochi chinakwera kufika pa 4,302. Tinachititsa maphunziro a Baibulo 140,403 m’mwezi wa March. Kunena zoona, Yehova anatamandika kwambiri pa miyezi itatu imeneyi. Tiyeni tipitirize kuchita zambiri mu ntchito ya Ambuye podziwa kuti zonse zimene tikuchita sizidzapita pachabe.—1 Akor. 15:58.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena