Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 January tsamba 4
  • Yehova Amakhululukira Munthu Amene Walapa Kuchokera Pansi pa Mtima

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amakhululukira Munthu Amene Walapa Kuchokera Pansi pa Mtima
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Yosiya Wodzichepetsayo Anayanjidwa Ndi Yehova
    Nsanja ya Olonda—2000
  • Mungachite Moyenera Ngakhale Sanakulereni Bwino
    Nsanja ya Olonda—2001
  • Kupereka Nsembe Zokondweretsa Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Yosiya Ankakonda Chilamulo cha Mulungu
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 January tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 2 MBIRI 33-36

Yehova Amakhululukira Munthu Amene Walapa Kuchokera Pansi pa Mtima

Losindikizidwa

MANASE

Yehova analola kuti amangidwe ndi Asuri n’kupita ku Babulo

Mfumu Manase ili ku ukapolo

MU ULAMULIRO WAKE ASANAMANGIDWE

  • Anamanga maguwa ansembe a milungu yonyenga

  • Anapereka nsembe ana ake

  • Anapha anthu osalakwa

  • Analimbikitsa zamizimu m’dziko lonse

MU ULAMULIRO WAKE ATAMASULIDWA

  • Anadzichepetsa kwambiri

  • Anapemphera kwa Yehova n’kupereka nsembe

  • Anawononga maguwa ansembe a milungu yonyenga

  • Analimbikitsa Aisiraeli onse kuti azitumikira Yehova

YOSIYA

Mfumu Yosiya

MU ULAMULIRO WAKE

  • Anafunafuna Yehova

  • Anayeretsa Yuda ndi Yerusalemu

  • Anakonza nyumba ya Yehova ndipo anapeza buku la Chilamulo

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena